Surah Al-Mulk ( Dominion ) - Aya 18

Surah Al-Mulk ( Dominion ) - Chewa - Aya 18 Aya count 30

وَلَقَدْ كَذَّبَ ٱلَّذِينَ مِن قَبْلِهِمْ فَكَيْفَ كَانَ نَكِيرِ ﴿١٨﴾
Ndithudi amene adalipo kale iwo asanabadwe adakana mithenga yawo. Nanga udali bwanji mkwiyo Wanga pa iwo (pakuwaononga onse)!
Share