Surah Al-An'am ( The Cattle ) - Aya 7

Surah Al-An'am ( The Cattle ) - Chewa - Aya 7 Aya count 165

وَلَوْ نَزَّلْنَا عَلَيْكَ كِتَٰبًۭا فِى قِرْطَاسٍۢ فَلَمَسُوهُ بِأَيْدِيهِمْ لَقَالَ ٱلَّذِينَ كَفَرُوٓا۟ إِنْ هَٰذَآ إِلَّا سِحْرٌۭ مُّبِينٌۭ ﴿٧﴾
Ndipo ngati tikadakutsitsira malemba (olembedwa) m’mapepala, (monga momwe adakufunsira), nkuwakhudza ndi manja awo, amene sadakhulupirire akadati: “Ichi sichina koma ndi matsenga owoneka.”
Share