Surah Al-Qamar ( The Moon ) - Aya 36

Surah Al-Qamar ( The Moon ) - Chewa - Aya 36 Aya count 55

وَلَقَدْ أَنذَرَهُم بَطْشَتَنَا فَتَمَارَوْا۟ بِٱلنُّذُرِ ﴿٣٦﴾
Ndipo ndithu (Luti) adawachenjeza anthu ake za kulanga Kwathu koopsa. Koma adakaikira machenjezo (ake ndi kumtsutsa).
Share