Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Aya 87

Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Chewa - Aya 87 Aya count 89

وَلَئِن سَأَلْتَهُم مَّنْ خَلَقَهُمْ لَيَقُولُنَّ ٱللَّهُ ۖ فَأَنَّىٰ يُؤْفَكُونَ ﴿٨٧﴾
Ndipo ngati utawafunsa: “Ndani adawalenga?” Anena motsimikiza kuti: “Ndi Allah.” Nanga akutembenuzidwa bwanji (kusiya choona)?
Share