Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Aya 81

Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Chewa - Aya 81 Aya count 89

قُلْ إِن كَانَ لِلرَّحْمَٰنِ وَلَدٌۭ فَأَنَا۠ أَوَّلُ ٱلْعَٰبِدِينَ ﴿٨١﴾
Nena (kwa omphatikiza Allah ndi mafano): “Zikadakhala kuti (Allah) Wachifundo chambiri ali ndi mwana, ndiye kuti ine ndikadakhala woyamba kumpembedza (mwanayo).”
Share