Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Aya 66

Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Chewa - Aya 66 Aya count 89

هَلْ يَنظُرُونَ إِلَّا ٱلسَّاعَةَ أَن تَأْتِيَهُم بَغْتَةًۭ وَهُمْ لَا يَشْعُرُونَ ﴿٦٦﴾
Palibe chimene akuyembekeza, koma Qiyâma basi yomwe iwadzera mwadzidzidzi pomwe iwo sakuzindikira (ali otanganidwa ndi za m’dziko).
Share