Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Aya 26

Surah Az-Zukhruf ( The Gold Adornment ) - Chewa - Aya 26 Aya count 89

وَإِذْ قَالَ إِبْرَٰهِيمُ لِأَبِيهِ وَقَوْمِهِۦٓ إِنَّنِى بَرَآءٌۭ مِّمَّا تَعْبُدُونَ ﴿٢٦﴾
Ndipo (kumbuka) pamene Ibrahim adauza bambo wake ndi anthu ake (kuti): “Ndithu ine ndadzipatula ku zimene mukuzipembedzazi.”
Share