Surah Ash-Shura (Consultation ) - Aya 34

Surah Ash-Shura (Consultation ) - Chewa - Aya 34 Aya count 53

أَوْ يُوبِقْهُنَّ بِمَا كَسَبُوا۟ وَيَعْفُ عَن كَثِيرٍۢ ﴿٣٤﴾
Kapena akhoza kuziononga (potumiza mphepo yamkuntho) chifukwa cha machimo amene adawachita. Koma amakhululuka zambiri.
Share