Surah Fussilat ( Explained in Detail ) - Aya 13

Surah Fussilat ( Explained in Detail ) - Chewa - Aya 13 Aya count 54

فَإِنْ أَعْرَضُوا۟ فَقُلْ أَنذَرْتُكُمْ صَٰعِقَةًۭ مِّثْلَ صَٰعِقَةِ عَادٍۢ وَثَمُودَ ﴿١٣﴾
Koma ngati anyozera (kukhulupirira), nena: “Ndikukuchenjezani za chilango monga chilango cha Âdi ndi Samud.”
Share