Surah An-Naml (The Ants ) - Aya 68

Surah An-Naml (The Ants ) - Chewa - Aya 68 Aya count 93

لَقَدْ وُعِدْنَا هَٰذَا نَحْنُ وَءَابَآؤُنَا مِن قَبْلُ إِنْ هَٰذَآ إِلَّآ أَسَٰطِيرُ ٱلْأَوَّلِينَ ﴿٦٨﴾
Ndithu tidalonjezedwa izi, ife ndi makolo athu kale, izi sichina koma ndi nthano (zabodza) za anthu akale.”
Share