Surah An-Naml (The Ants ) - Aya 67

Surah An-Naml (The Ants ) - Chewa - Aya 67 Aya count 93

وَقَالَ ٱلَّذِينَ كَفَرُوٓا۟ أَءِذَا كُنَّا تُرَٰبًۭا وَءَابَآؤُنَآ أَئِنَّا لَمُخْرَجُونَ ﴿٦٧﴾
Ndipo adanena omwe adatsutsa (za Allah): “Kodi tikadzakhala dothi, ife ndi makolo athu akale, (nzoona) tidzatulutsidwanso (m’manda tili amoyo)?”
Share