Surah An-Naml (The Ants ) - Aya 54

Surah An-Naml (The Ants ) - Chewa - Aya 54 Aya count 93

وَلُوطًا إِذْ قَالَ لِقَوْمِهِۦٓ أَتَأْتُونَ ٱلْفَٰحِشَةَ وَأَنتُمْ تُبْصِرُونَ ﴿٥٤﴾
Ndipo (akumbutse nkhani ya) Luti pamene adanena kwa anthu ake: “Kodi mukuchita zadama uku inu mukuziona?”
Share