Surah An-Naml (The Ants ) - Aya 38

Surah An-Naml (The Ants ) - Chewa - Aya 38 Aya count 93

قَالَ يَٰٓأَيُّهَا ٱلْمَلَؤُا۟ أَيُّكُمْ يَأْتِينِى بِعَرْشِهَا قَبْلَ أَن يَأْتُونِى مُسْلِمِينَ ﴿٣٨﴾
(Sulaiman adasonkhanitsa nduna zake) nati: “E inu nduna! Ndani abwere ndi mpando wake wachifumuwo kwa ine asadandidzere ali ogonja?”
Share