Surah Maryam ( Mary ) - Aya 88

Surah Maryam ( Mary ) - Chewa - Aya 88 Aya count 98

وَقَالُوا۟ ٱتَّخَذَ ٱلرَّحْمَٰنُ وَلَدًۭا ﴿٨٨﴾
Ndipo (osakhulupirira omwe ndi Ayuda ndi Akhirisitu) akuti: “(Allah) Mwini chifundo chambiri wadzipangira mwana!”
Share