Surah Al-Isra ( The Night Journey ) - Aya 103

Surah Al-Isra ( The Night Journey ) - Chewa - Aya 103 Aya count 111

فَأَرَادَ أَن يَسْتَفِزَّهُم مِّنَ ٱلْأَرْضِ فَأَغْرَقْنَٰهُ وَمَن مَّعَهُۥ جَمِيعًۭا ﴿١٠٣﴾
Choncho (Farawo) adafuna kuwatulutsa m’dziko (la Iguputo Mûsa ndi ana a Israyeli) koma tidammiza iye ndi onse omwe adali naye.
Share