Surah An-Nas ( Mankind )

Surah An-Nas ( Mankind ) - Chewa Aya count 6

Nena: “Ndikudzitchinjiriza ndi Mbuye (Mleri) wa anthu (Yemwe akulinganiza zinthu zawo).[503]
Mfumu ya anthu ( Imene iri ndi mphamvu yochita chirichonse pa iwo).
Kuzoipa za mnong’onezi (yemwe amathira unong’onezi wake m’mitimaya anthu) yemwenso amabisala (posiya unong’onezi wake ngati mwini mtimawo atankumbukira Allah).[504]
Wochokera m’ziwanda ndi mwa anthu.”[505]
Share