Surah Al-Falaq ( The Daybreak )

Surah Al-Falaq ( The Daybreak ) - Chewa Aya count 5

Nena: “Ndikudzitchinjiriza ndi Mbuye wam’bandakucha.[499]
Kuchokera ku zoipa zimene Iye adazilenga.[500]
Ndi ku zoipa za usiku pamene mdima ukulowa mwa mphamvu.[501]
Ndiponso ku zoipa za wansanje pamene akuchita nsanje.”[502]
Share