Surah Al-Kafiroon ( The Disbelievers ) - Aya 4

Surah Al-Kafiroon ( The Disbelievers ) - Chewa - Aya 4 Aya count 6

وَلَآ أَنَا۠ عَابِدٌۭ مَّا عَبَدتُّمْ ﴿٤﴾
Ndiponso ine sindidzapembedza chimene inu mwakhala mukuchipembedza (chifukwa inu ndinu ophatikiza Allah ndi zinthu zina).
Share