Surah Al-Asr ( The Time )

Surah Al-Asr ( The Time ) - Chewa Aya count 3

Ndikuilumbilira nthawi.[480]
Ndithu munthu aliyense ndi wotaika (chifukwa chakugonjetsedwa ndi zilakolako zake).
Kupatula amene akhulupirira (mwa Allah) ndi kumachita zabwino, ndikumalangizana kutsatira choona ndiponso ndi kumalangizana za kupirira (potsatira malamulo a Allah ndi zina za mdziko).[481]
Share