Surah At-Takathur ( The piling Up )

Surah At-Takathur ( The piling Up ) - Chewa Aya count 8

Kwakutangwanitsani kusonkhanitsa (chuma chambiri ndi ana).[477]
Mpakana mwapita kumanda (mwamwalira ndikukalowa m’manda).
Sichoncho! mukadakhala mukudziwa, kudziwa kwachitsimikizo (sibwenzi mukutangwanika ndi za mdziko).
Tsono patsikulo ndithudi mudzafunsidwa za mtendere (omwe munapatsidwa).[479]
Share